Kodi katemera angathandize bwanji kupewa chiwewe cha agalu?
Chiwewe ndi nthenda yowopsa kwambiri m'madera ambiri amu Afilika. Ngakhale zili choncho, ndiyopeweka kudzera mu katemera. Katemera amateteza agalu ndikuwakanikitsa kufalitsa matendawa kwa zinyama zina, inde ngakhalenso kwa anthu.
| Main Author: | |
|---|---|
| Format: | Video |
| Language: | ny |
| Published: |
International Livestock Research Institute
2023
|
| Subjects: | |
| Online Access: | https://hdl.handle.net/10568/131546 |
Similar Items: Kodi katemera angathandize bwanji kupewa chiwewe cha agalu?
- Je, chanjo inawezaje kuzuia kichaa cha mbwa kwa mbwa?
- Nzanzo îtonya ata kúsiîa mûng'ethya ngitînî?
- Comment la vaccination peut-elle prévenir la rage chez le chien?
- How rabies infection occurs
- How can vaccination prevent rabies in dogs?
- Demography of owned dogs across an East African continuum of high-low human density