Kodi katemera angathandize bwanji kupewa chiwewe cha agalu?

Chiwewe ndi nthenda yowopsa kwambiri m'madera ambiri amu Afilika. Ngakhale zili choncho, ndiyopeweka kudzera mu katemera. Katemera amateteza agalu ndikuwakanikitsa kufalitsa matendawa kwa zinyama zina, inde ngakhalenso kwa anthu.

Bibliographic Details
Main Author: International Livestock Research Institute
Format: Video
Language:ny
Published: International Livestock Research Institute 2023
Subjects:
Online Access:https://hdl.handle.net/10568/131546
Description
Summary:Chiwewe ndi nthenda yowopsa kwambiri m'madera ambiri amu Afilika. Ngakhale zili choncho, ndiyopeweka kudzera mu katemera. Katemera amateteza agalu ndikuwakanikitsa kufalitsa matendawa kwa zinyama zina, inde ngakhalenso kwa anthu.